Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 73:10 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake anthu ake amabwera kudza kuno, ndipo chikho chodzala ndi madzi achigugudiza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake anthu ake amabwera kudza kuno, ndipo chikho chodzala ndi madzi achigugudiza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake ngakhale anthu a Mulungu amabwera kwa iwo, ndipo amakhuta zonena zao ngati madzi akumwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼchifukwa chake anthu awo amapita kwa iwowo ndi kumwa madzi mochuluka.

Onani mutuwo



Masalimo 73:10
1 Mawu Ofanana  

Pakuti m'dzanja la Yehova muli chikho; ndi vinyo wake achita thovu; chidzala ndi zosakanizira, ndipo atsanulako. Indedi, oipa onse a padziko lapansi adzamwa nadzagugudiza nsenga zake.