Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 72:20 - Buku Lopatulika

Mapemphero a Davide mwana wa Yese atha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mapemphero a Davide mwana wa Yese atha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ano ndiwo mathero a mapemphero a Davide, mwana wa Yese.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Uku ndiko kumaliza kwa mapemphero a Davide mwana wa Yese.

Onani mutuwo



Masalimo 72:20
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mau otsiriza a Davide ndi awa: Atero Davide mwana wa Yese, atero munthu wokwezedwa, ndiye wodzozedwa wa Mulungu wa Yakobo, ndi mwini nyimbo yokoma ya Israele.


imere minga m'malo mwa tirigu, ndi dawi m'malo mwa barele. Mau a Yobu atha.


nuti, Chomwecho adzamira Babiloni, sadzaukanso chifukwa cha choipa chimene ndidzamtengera iye; ndipo adzatopa. Mau a Yeremiya ndi omwewo.


Ndipo kunali, pakuwadalitsa Iye analekana nao, natengedwa kunka Kumwamba.