Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 72:13 - Buku Lopatulika

Adzachitira nsoni wosauka ndi waumphawi, nadzapulumutsa moyo wa aumphawi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Adzachitira nsoni wosauka ndi waumphawi, nadzapulumutsa moyo wa aumphawi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Idzamvera chisoni anthu ofooka ndi osoŵa, ndipo idzapulumutsa moyo wa anthu aumphaŵi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye adzachitira chifundo anthu ofowoka ndi anthu osowa ndi kupulumutsa osowa ku imfa.

Onani mutuwo



Masalimo 72:13
6 Mawu Ofanana  

Popeza adzaima padzanja lamanja la waumphawi, kumpulumutsa kwa iwo akuweruza koipa moyo wake.


Ndidzafuna yotayika, ndi kubweza yopirikitsidwa, ndi kulukira chika yothyoka mwendo, ndikulimbitsa yodwalayo; koma yonenepa ndi yolimba ndidzaziononga, ndidzazidyetsa ndi chiweruzo.


Yang'anirani kuti musanyoze mmodzi wa ang'ono awa; pakuti ndinena kwa inu, kuti angelo ao apenya chipenyere nkhope ya Atate wanga wa Kumwamba.


Odala ali osauka mumzimu; chifukwa uli wao Ufumu wa Kumwamba.