Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 7:14 - Buku Lopatulika

Taonani, ali m'chikuta cha zopanda pake; anaima ndi chovuta, nabala bodza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Taonani, ali m'chikuta cha zopanda pake; anaima ndi chovuta, nabala bodza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zoonadi, munthu woipa amalingalira zoipa zokhazokha nthaŵi zonse, ntchito yake ndi kunyenga ndi kuvutitsa anthu ena basi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Taonani, munthu woyipa amalingalira zoyipa zokhazokha nthawi zonse. Zochita zake ndi zosokoneza ndi zovutitsa anthu ena.

Onani mutuwo



Masalimo 7:14
6 Mawu Ofanana  

Munthu woipa adzipweteka masiku ake onse, ndi zaka zowerengeka zisingikira woopsa.


Aima ndi chovuta, nabala mphulupulu, ndi m'mimba mwao mukonzeratu chinyengo.


Inu mudzatenga pakati ndi mungu, mudzabala ziputu; mpweya wanu ndi moto umene udzakumalizani inu.


Ndidzawaunjikira zoipa; ndidzawathera mivi yanga.


Pamenepo chilakolakocho chitaima, chibala uchimo; ndipo uchimo, utakula msinkhu, ubala imfa.