Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:5 - Buku Lopatulika

Mulungu, mudziwa kupusa kwanga; ndipo kutsutsika kwanga sikubisikira Inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mulungu, mudziwa kupusa kwanga; ndipo kutsutsika kwanga sikubisikira Inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, mumadziŵa kupusa kwanga, zolakwa zanga sizili zobisika pamaso panu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mukudziwa uchitsiru wanga, Inu Mulungu, kulakwa kwanga sikuli kobisika kwa Inu.

Onani mutuwo



Masalimo 69:5
7 Mawu Ofanana  

Mwayesera mtima wanga; mwandizonda usiku; mwandisuntha, simupeza kanthu; mwatsimikiza mtima kuti m'kamwa mwanga simudzalakwa.


Adziwitsa zolowereza zake ndani? Mundimasule kwa zolakwa zobisika.


Adani anga asandikondwerere ine monyenga; okwiya nane kopanda chifukwa asanditsinzinire.


Mabala anga anunkha, adaola, chifukwa cha kupusa kwanga.


Ambuye, chikhumbo changa chonse chili pamaso panu; ndipo kubuula kwanga sikubisika kwa Inu.


Pakuti maso anga ali panjira zao zonse, sabisika pa nkhope yanga, mphulupulu yao siibisika pamaso panga.