Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:31 - Buku Lopatulika

Ndipo chidzakomera Yehova koposa ng'ombe, inde mphongo za nyanga ndi ziboda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo chidzakomera Yehova koposa ng'ombe, inde mphongo za nyanga ndi ziboda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zimenezi zidzakondwetsa Chauta kupambana nsembe, ngakhale nsembe ya ng'ombe yamphongo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Izi zidzakondweretsa Yehova kupambana ngʼombe, kupambananso ngʼombe yayimuna, pamodzi ndi nyanga ndi ziboda zake.

Onani mutuwo



Masalimo 69:31
6 Mawu Ofanana  

Wopereka nsembe yachiyamiko andilemekeza Ine; ndipo kwa iye wosunga mayendedwe ake ndidzamuonetsa chipulumutso cha Mulungu.


Mukani nao mau, nimubwerere kwa Yehova; nenani kwa Iye, Chotsani mphulupulu zonse, nimulandire chokoma; ndipo tidzapereka mau milomo yathu ngati ng'ombe.


Potero mwa Iye tipereke chiperekere nsembe yakuyamika Mulungu, ndiyo chipatso cha milomo yovomereza dzina lake.


inunso ngati miyala yamoyo mumangidwa nyumba ya uzimu, kuti mukhale ansembe oyera mtima, akupereka nsembe zauzimu, zolandiridwa ndi Mulungu mwa Yesu Khristu.