Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:26 - Buku Lopatulika

Pakuti alondola amene Inu munampanda; ndipo akambirana za zowawa zao za iwo amene munawalasa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti alondola amene Inu munampanda; ndipo akambirana za zowawa zao za iwo amene munawalasa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo amazunza amene Inu mwamkantha, ndipo amene Inu mwamupweteka, iwo amaonjezera kumuvutitsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti iwo amazunza amene inu munamuvulaza ndi kuyankhula zowawa kwa amene munawapweteka.

Onani mutuwo



Masalimo 69:26
10 Mawu Ofanana  

Koma panali mneneri wa Yehova pomwepo, dzina lake Odedi; natuluka iye kukomana nayo nkhondo ikudzayo ku Samariya, nanena nao, Taonani, popeza Yehova Mulungu wa makolo anu anakwiya ndi Yuda, anawapereka m'dzanja lanu, nimunawapha ndi kupsa mtima kofikira kumwamba.


Aipsa njira yanga, athandizana ndi tsoka langa; ndiwo anthu omwewo osowa mthandizi.


Chifukwa kuti sanakumbukire kuchita chifundo, koma analondola wozunzika ndi waumphawi, ndi wosweka mtima, kuti awaphe.


Koma kunakomera Yehova kumtundudza; anammvetsa zowawa; moyo wake ukapereka nsembe yopalamula, Iye adzaona mbeu yake, adzatanimphitsa masiku ake; ndipo chomkondweretsa Yehova chidzakula m'manja mwake.


Zoonadi Iye ananyamula zowawa zathu, ndi kusenza zisoni zathu; koma ife tinamuyesa wokhomedwa, wokanthidwa ndi Mulungu, ndi wovutidwa.


Ndipo ndikwiya nao amitundu okhala osatekeseka ndi mkwiyo waukulu; pakuti ndinakwiya pang'ono, ndipo anathandizira choipa.


Galamuka, lupanga, pa mbusa wanga, ndi pa munthu mnzanga wa pamtima, ati Yehova wa makamu; kantha mbusa, ndi nkhosa zidzabalalika; koma ndidzabwezera dzanja langa pa zazing'onozo.


amene adaphanso Ambuye Yesu, ndi aneneri, natilondalonda ife, ndipo sakondweretsa Mulungu, natsutsana nao anthu onse;