Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:22 - Buku Lopatulika

Gome lao likhale msampha pamaso pao; pokhala ndi mtendere iwo, likhale khwekhwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Gome lao likhale msampha pamaso pao; pokhala ndi mtendere iwo, likhale khwekhwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zakudya zao zisanduke msampha. Akodwe ndi maphwando a nsembe zao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chakudya chomwe chayikidwa patsogolo pawo chikhale msampha; chikhale chobwezera chilango ndiponso khwekhwe.

Onani mutuwo



Masalimo 69:22
7 Mawu Ofanana  

Pakuti kubwerera m'mbuyo kwa achibwana kudzawapha; ndipo mphwai za opusa zidzawaononga.


Mukapanda kumvera, mukapanda kuliika mumtima mwanu, kupatsa dzina langa ulemerero, ati Yehova wa makamu, ndidzakutumizirani temberero, ndi kutemberera madalitso anu; inde, ndawatemberera kale chifukwa simuliika mumtima.


Lidzakhala lotembereredwa dengu lanu ndi choumbiramo mkate wanu.


Pamene angonena, Mtendere ndi mosatekeseka, pamenepo chionongeko chobukapo chidzawagwera, monga zowawa mkazi wa pakati; ndipo sadzapulumuka konse.


Ndipo, Mwala wakukhumudwa nao, ndi thanthwe lophunthwitsa. Kwa iwo akukhumudwa ndi mau, pokhala osamvera, kumenekonso adaikidwako.