Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 69:15 - Buku Lopatulika

Chigumula chisandifotsere, ndipo chakuya chisandimize; ndipo asanditsekere pakamwa pake pa dzenje.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chigumula chisandifotsere, ndipo chakuya chisandimize; ndipo asanditsekere pakamwa pake pa dzenje.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Musalole kuti chigumula chindikokolole, kapena kuti nyanja yakuya indimize. Musalole kuti manda atseke kukamwa atandimeza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musalole kuti chigumula chindimeze, kuya kusandimeze ndipo dzenje lisatseke pakamwa pake kundimiza.

Onani mutuwo



Masalimo 69:15
11 Mawu Ofanana  

Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu padziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi.


Pakuti simudzasiya moyo wanga kumanda; simudzalola wokondedwa wanu avunde.


pakuti monga Yona anali m'mimba mwa chinsomba masiku atatu ndi usiku wake, chomwecho Mwana wa Munthu adzakhala mumtima mwa dziko lapansi masiku atatu ndi usiku wake.


yemweyo Mulungu anamuukitsa, atamasula zowawa za imfa, mwakuti sikunali kotheka kuti Iye agwidwe nayo.


iye pakuona ichi kale, analankhula za kuuka kwa Khristu, kuti sanasiyidwe m'dziko la akufa, ndipo thupi lake silinaone chivunde.