Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 66:18 - Buku Lopatulika

Ndikadasekera zopanda pake m'mtima mwanga, Ambuye sakadamvera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikadasekera zopanda pake m'mtima mwanga, Ambuye sakadamvera.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikadazindikira choipa chilichonse mumtima mwanga ndi kuchibisa, Ambuye sakadandimvera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndikanasekerera tchimo mu mtima mwanga Ambuye sakanamvera;

Onani mutuwo



Masalimo 66:18
10 Mawu Ofanana  

Zedi Mulungu samvera zachabe, ndi Wamphamvuyonse sazisamalira.


Chenjerani, musalunjike kumphulupulu; pakuti mwaisankha iyi mutazunzidwa.


Yehova atalikira oipa; koma pemphero la olungama alimvera.


Nsembe ya oipa inyansa Yehova; koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.


Wotseka makutu ake polira waumphawi, nayenso adzalira koma osamvedwa.


Wopewetsa khutu lake kuti asamve chilamulo, ngakhale pemphero lake linyansa.


Ndipo pamene mutambasula manja anu, ndidzakubisirani inu maso anga; inde pochulukitsa mapemphero anu Ine sindidzamva; manja anu adzala mwazi.


Tidziwa kuti Mulungu samvera ochimwa. Koma ngati munthu aliyense akhala wopembedza Mulungu nachita chifuniro chake, amvera ameneyo.


Mupempha, ndipo simulandira, popeza mupempha koipa, kuti mukachimwaze pochita zikhumbitso zanu.