Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 66:11 - Buku Lopatulika

Munapita nafe kuukonde; munatisenza chothodwetsa pamsana pathu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munapita nafe kuukonde; munatisenza chothodwetsa pamsana pathu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu mudatiloŵetsa mu ukonde wa adani, mudatisenzetsa katundu wolemera pamsana pathu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mwatilowetsa mʼndende ndi kutisenzetsa zolemera pa misana yathu.

Onani mutuwo



Masalimo 66:11
7 Mawu Ofanana  

Dziwani tsopano kuti Mulungu wandikhotetsera mlandu wanga, nandizinga ndi ukonde wake.


Anatumiza moto wochokera kumwamba kulowa m'mafupa anga, unawagonjetsa; watchera mapazi anga ukonde, wandibwezera m'mbuyo; wandipululutsa ndi kundilefula tsiku lonse.


Ndidzamphimba ndi ukonde wanga, nadzakodwa iye mu msampha wanga; ndipo ndidzafika naye ku Babiloni, ku dziko la Ababiloni; sadzaliona, chinkana adzafako.


Pamene amuka ndidzawayalira ukonde wanga, ndidzawagwetsa ngati mbalame za m'mlengalenga, ndidzawalanga monga udamva msonkhano wao.


Ndipo musatitengere kokatiyesa, koma mutipulumutse kwa woipayo.


Dalitsani, Yehova, mphamvu yake, nimulandire ntchito ya manja ake; akantheni m'chuuno iwo akumuukira, ndi iwo akumuda, kuti asaukenso.