Yehova ndiye gawo la cholowa changa ndi chikho changa, ndinu wondigwirira cholandira changa.
Masalimo 61:6 - Buku Lopatulika Mudzatalikitsa moyo wa mfumu. Zaka zake zidzafikira mibadwomibadwo. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Mudzatalikitsa moyo wa mfumu. Zaka zake zidzafikira mibadwomibadwo. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Talikitsani moyo wa mfumu, zaka zake zifikire ku mibadwo ndi mibadwo. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu, zaka zake kwa mibado yochuluka. |
Yehova ndiye gawo la cholowa changa ndi chikho changa, ndinu wondigwirira cholandira changa.
Koma kunakomera Yehova kumtundudza; anammvetsa zowawa; moyo wake ukapereka nsembe yopalamula, Iye adzaona mbeu yake, adzatanimphitsa masiku ake; ndipo chomkondweretsa Yehova chidzakula m'manja mwake.