Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 61:5 - Buku Lopatulika

Pakuti Inu, Mulungu, mudamva zowinda zanga; munandipatsa cholowa cha iwo akuopa dzina lanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti Inu, Mulungu, mudamva zowinda zanga; munandipatsa cholowa cha iwo akuopa dzina lanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, mwamva zimene ndalumbira popemphera. Inu mwandipatsa choloŵa chimene amalandira anthu oopa dzina lanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga; mwandipatsa cholowa cha iwo amene amaopa dzina lanu.

Onani mutuwo



Masalimo 61:5
10 Mawu Ofanana  

Adzadalitsa iwo akuopa Yehova, aang'ono ndi aakulu.


Ndisungeni monga kamwana ka m'diso, ndifungatireni mu mthunzi wa mapiko anu,


Zowindira Inu Mulungu, zili pa ine, ndidzakuchitirani zoyamika.


Mu Ziyoni akulemekezani Inu mwachete, Mulungu, adzakuchitirani Inu chowindachi.


Koma Mulungu anamvadi; anamvera mau a pemphero langa.


Mundionetse njira yanu, Yehova; ndidzayenda m'choonadi chanu, muumbe mtima wanga ukhale umodzi kuti uliope dzina lanu.


Ndidzati kwa Yehova, Pothawirapo panga ndi linga langa; Mulungu wanga, amene ndimkhulupirira.


koma m'mitundu yonse, wakumuopa Iye ndi wakuchita chilungamo alandiridwa naye.