Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 61:1 - Buku Lopatulika

Imvani mfuu wanga, Mulungu; mverani pemphero langa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Imvani mfuu wanga, Mulungu; mverani pemphero langa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, imvani kulira kwanga, mverani pemphero langa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu; mvetserani pemphero langa.

Onani mutuwo



Masalimo 61:1
11 Mawu Ofanana  

Ambuye, imvani liu langa; makutu anu akhale chimverere mau a kupemba kwanga.


Yehova, imvani chilungamo, mverani mfuu wanga; tcherani khutu ku pemphero langa losatuluka m'milomo ya chinyengo.


Mverani mau a kupemba kwanga, pamene ndilirira Inu, pamene ndikweza manja anga kuloza ponenera panu poyera.


Pakufuula ine mundiyankhe, Mulungu wa chilungamo changa; pondichepera mwandikulitsira malo. Ndichitireni chifundo, imvani pemphero langa.


Ndipulumutseni, Mulungu, mwa dzina lanu, ndipo mundiweruze ndi mphamvu yanu.


Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, ndipo musandilange muukali wanu.


Imvani Mulungu, mau anga, m'kudandaula kwanga; sungani moyo wanga angandiopse mdani.


Tcherani khutu pemphero langa, Yehova; nimumvere mau a kupemba kwanga.


Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.