Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 60:9 - Buku Lopatulika

Adzandifikitsa ndani m'mzinda wa m'linga? Adzanditsogolera ndani ku Edomu?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Adzandifikitsa ndani m'mudzi wa m'linga? Adzanditsogolera ndani ku Edomu?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndani adzandifikitse ku mzinda wamalinga? Ndani adzanditsogolere ku Edomu?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Adzandifikitse ndani ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?

Onani mutuwo



Masalimo 60:9
7 Mawu Ofanana  

Ndodo yachifumu siidzachoka mwa Yuda, kapena wolamulira pakati pa mapazi ake, kufikira atadza Silo; ndipo anthu adzamvera iye.


Ndipo kunali pofikanso chaka, nyengo yakutuluka mafumu, Davide anatumiza Yowabu, pamodzi ndi anyamata ake, ndi Aisraele onse; ndipo iwo anasakaza ana a Amoni, naumangira misasa yankhondo Raba. Koma Davide anatsalira ku Yerusalemu.


Nati Davide, Aliyense woyamba kukantha Ayebusi, yemweyo adzakhala mkulu ndi mtsogoleri. Nayamba kukwerako Yowabu mwana wa Zeruya, nakhala mkulu iyeyu.


Ndipo Kalebe anati, Iye amene akantha mudzi wa Kiriyati-Sefere, naulanda, yemweyo ndidzampatsa Akisa mwana wanga wamkazi akhale mkazi wake.