Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 59:6 - Buku Lopatulika

Abwera madzulo, auwa ngati galu, nazungulira mzinda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Abwera madzulo, auwa ngati galu, nazungulira mudzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amabweranso madzulo aliwonse akuuwa ngati agalu, nkumangoyendayenda mu mzinda.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iwo amabweranso madzulo akuchita phokoso ngati agalu ndi kumangoyendayenda mu mzinda.

Onani mutuwo



Masalimo 59:6
4 Mawu Ofanana  

Muwakumbukire Mulungu wanga, popeza anadetsa unsembe, ndi pangano la unsembe, ndi la Alevi.


Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga.


Ndipo abwere madzulo, auwe ngati galu, nazungulire mzinda.


Ndipo Saulo anatumiza mithenga kunyumba ya Davide imdikire, ndi kumupha m'mawa; koma Mikala mkazi wa Davide anamuuza, nati, Ukapanda kupulumutsa moyo wako usiku uno, udzaphedwa ndithu m'mawa.