Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 56:3 - Buku Lopatulika

Tsiku lakuopa ine, ndidzakhulupirira Inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsiku lakuopa ine, ndidzakhulupirira Inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene ndichita mantha ndimadalira Inu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndikachita mantha ndimadalira Inu.

Onani mutuwo



Masalimo 56:3
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehosafati anachita mantha, nalunjikitsa nkhope yake kufuna Yehova, nalalikira kusala mwa Ayuda onse.


Ndakhulupirira Yehova, mutani nkunena kwa moyo wanga, Thawirani kuphiri lanu ngati mbalame?


Ndinafuna Yehova ndipo anandivomera, nandilanditsa m'mantha anga onse.


Ndipo Davide ananyamuka, nathawa tsiku lomwelo chifukwa cha kuopa Saulo, namuka kwa Akisi mfumu ya ku Gati.


Ndipo Davide anasunga mau awa mumtima mwake, naopa kwambiri Akisi mfumu ya Gati.


Ndipo Davide anadololoka kwambiri, pakuti anthu ananena za kumponya iye miyala, pakuti mtima wao wa anthu onse unali ndi chisoni, yense chifukwa cha ana ake aamuna ndi aakazi. Koma Davide anadzilimbikitsa mwa Yehova Mulungu wake.