Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 54:2 - Buku Lopatulika

Imvani pemphero langa, Mulungu; tcherani khutu mau a pakamwa panga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Imvani pemphero langa, Mulungu; tcherani khutu mau a pakamwa panga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, imvani pemphero langa, tcherani khutu kuti mumve mau a pakamwa panga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imvani pemphero langa, Inu Mulungu mvetserani mawu a pakamwa panga.

Onani mutuwo



Masalimo 54:2
7 Mawu Ofanana  

Penyani, ndiyankheni, Yehova Mulungu wanga. Penyetsani maso anga, kuti ndingagone tulo ta imfa;


Ambuye, imvani liu langa; makutu anu akhale chimverere mau a kupemba kwanga.


Fulumirani ndiyankheni, Yehova; mzimu wanga ukutha. Musandibisire nkhope yanu; ndingafanane nao akutsikira kudzenje.


Ndipo a ku Zifi anakwera kwa Saulo ku Gibea, nati, Davide salikubisala kwathu kodi, m'ngaka za m'nkhalango ku Horesi, m'phiri la Hakila, limene lili kumwera kwa chipululu?


Ndipo Azifi anafika kwa Saulo ku Gibea, nati, Kodi Davide sali kubisala m'phiri la Hakila, kupenya kuchipululu!