ukonda mau onse akuononga, lilime lachinyengo, iwe.
Umakonda kulankhula mau ovutitsa ena, iwe wabodzawe.
Umakonda mawu onse opweteka, iwe lilime lachinyengo!
Adzakuninkhanji, adzakuonjezeranji, lilime lonyenga iwe?
Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.
Pakamwa pako mpochita zochimwa, ndipo lilime lako likonza chinyengo.