Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 52:4 - Buku Lopatulika

ukonda mau onse akuononga, lilime lachinyengo, iwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ukonda mau onse akuononga, lilime lachinyengo, iwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Umakonda kulankhula mau ovutitsa ena, iwe wabodzawe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Umakonda mawu onse opweteka, iwe lilime lachinyengo!

Onani mutuwo



Masalimo 52:4
5 Mawu Ofanana  

Adzakuninkhanji, adzakuonjezeranji, lilime lonyenga iwe?


Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.


Pakamwa pako mpochita zochimwa, ndipo lilime lako likonza chinyengo.