Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 50:9 - Buku Lopatulika

Sindidzatenga ng'ombe m'nyumba mwako, kapena mbuzi m'makola mwako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Sindidzatenga ng'ombe m'nyumba mwako, kapena mbuzi m'makola mwako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndithudi, sindilandira ng'ombe kapena mbuzi iliyonse ya m'makola anu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,

Onani mutuwo



Masalimo 50:9
6 Mawu Ofanana  

Pamenepo ndinati, Taonani, ndadza; m'buku mwalembedwa za Ine,


Ndipo chidzakomera Yehova koposa ng'ombe, inde mphongo za nyanga ndi ziboda.


satumikiridwa ndi manja a anthu, monga wosowa kanthu, popeza Iye mwini apatsa zonse moyo ndi mpweya ndi zinthu zonse;