Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 49:9 - Buku Lopatulika

Kuti akhale ndi moyo osafa, osaona chivundi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kuti akhale ndi moyo osafa, osaona chivundi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kuti azikhalabe ndi moyo mpaka muyaya osapita ku manda.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuti iye akhale ndi moyo mpaka muyaya ndi kusapita ku manda.

Onani mutuwo



Masalimo 49:9
13 Mawu Ofanana  

Pakuti simudzasiya moyo wanga kumanda; simudzalola wokondedwa wanu avunde.


Onenepa onse a padziko lapansi adzadya nadzagwadira; onse akutsikira kufumbi adzawerama pamaso pake, ndi iye amene sadziwa kusunga moyo wake.


Munthu ndani amene adzakhalabe ndi moyo, osaona imfa? Amene adzapulumutsa moyo wake kumphamvu ya manda?


Chuma cha uchimo sichithangata; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa.


Chuma sichithandiza tsiku la mkwiyo; koma chilungamo chipulumutsa kuimfa.


Kulibe munthu ali ndi mphamvu yolamulira mzimu ndi yakutsekereza mzimu; ngakhale mphamvu tsiku la imfa; munkhondo umo mulibe kumasuka; udyo sudzapulumutsa akuzolowerana nao.


Makolo anu, ali kuti iwowo? Ndi aneneri, akhala ndi moyo kosatha kodi?


kuti Mulungu analikwaniritsa ili kwa ana athu pakuukitsa Yesu; monganso mulembedwa mu Salimo lachiwiri, Iwe ndiwe Mwana wanga, lero ndakubala.


Pakuti simudzasiya moyo wanga ku dziko la akufa, kapena simudzapereka Woyera wanu aone chivunde,


iye pakuona ichi kale, analankhula za kuuka kwa Khristu, kuti sanasiyidwe m'dziko la akufa, ndipo thupi lake silinaone chivunde.