Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 49:8 - Buku Lopatulika

Popeza chiombolo cha moyo wao ncha mtengo wake wapatali, ndipo chilekeke nthawi zonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Popeza chiombolo cha moyo wao ncha mtengo wake wapatali, ndipo chilekeke nthawi zonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Popeza kuti choombolera moyo wa munthu ndi chamtengowapatali, ndipo sangathe kuchikwanitsa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dipo la moyo ndi la mtengowapatali, palibe malipiro amene angakwanire,

Onani mutuwo



Masalimo 49:8
4 Mawu Ofanana  

Kapena, Mundilanditse m'dzanja la mdani? Kapena, Mundiombole m'dzanja la oopsa?


Chilikuti chifundo chanu chakale, Ambuye, munachilumbirira Davide pa chikhulupiriko chanu?


Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake?