Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 49:2 - Buku Lopatulika

awamba ndi omveka omwe, achuma ndi aumphawi omwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

awamba ndi omveka omwe, achuma ndi aumphawi omwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

anthu otsika ndi okwera omwe, olemera ndi osauka omwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

anthu wamba pamodzi ndi anthu odziwika, olemera pamodzinso ndi osauka:

Onani mutuwo



Masalimo 49:2
10 Mawu Ofanana  

Nanga kwa Iye wosasamalira nkhope za akalonga, wosasiyanitsa pakati pa wolemera ndi wosauka? Pakuti onsewo ndiwo ntchito ya manja ake.


Indetu, anthu achabe ndi mpweya, ndipo anthu aakulu ndi bodza, pakuwayesa apepuka; onse pamodzi apepuka koposa mpweya.


Wolemera ndi wosauka akumana, wolenga onsewo ndiye Yehova.


Idzani pafupi, amitundu inu, kuti mumve; mverani anthu inu, dziko ndi zinthu zonse zotulukamo.


Imvani, mitundu ya anthu, inu nonse; tamvera, dziko lapansi, ndi zonse zili m'mwemo; ndipo Ambuye Yehova akhale mboni yakutsutsa inu, Ambuye mu Kachisi wake wopatulika.