Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 48:4 - Buku Lopatulika

Pakuti, taonani, mafumuwo anasonkhana, anapitira pamodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti, taonani, mafumuwo anasonkhana, anapitira pamodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mafumu adasonkhana, adafuna kuuthira nkhondo pamodzi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,

Onani mutuwo



Masalimo 48:4
12 Mawu Ofanana  

Koma mtima wa mfumu ya Aramu unavutika kwambiri pa ichicho, naitana anyamata ake, nanena nao, Kodi simudzandiuza wina wa ife wovomerezana ndi mfumu ya Israele ndani?


Popeza ati, Akalonga anga kodi sali onse mafumu?


Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ake ovutidwa adzaona pobisalira.


Tsiku limenelo adzaimba nyimbo imeneyi m'dziko la Yuda, Ife tili ndi mzinda wolimba; Iye adzaika chipulumutso chikhale machemba ndi malinga.


Ndipo panali masiku a Ahazi, mwana wa Yotamu, mwana wa Uziya, mfumu ya Yuda, kuti Rezini, mfumu ya Aramu, ndi Peka, mwana wa Remaliya, mfumu ya Israele, anakwera kunka ku Yerusalemu, kumenyana nao; koma sanathe kuupambana.


Ndipo chinagwidwa chilombocho, ndi pamodzi nacho mneneri wonyenga amene adachita zizindikiro pamaso pake, zimene anasokeretsa nazo iwo amene adalandira lemba la chilombo, ndi iwo akulambira fano lake; iwo awiri anaponyedwa ali moyo m'nyanja yamoto yakutentha ndi sulufure: