Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 48:12 - Buku Lopatulika

Zungulirani Ziyoni, ndipo muuzinge, werengani nsanja zake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zungulirani Ziyoni, ndipo muuzinge, werengani nsanja zake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zungulirani Ziyoni yense, inde zungulirani mzinda wonsewo, ndipo muŵerenge nsanja zake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.

Onani mutuwo



Masalimo 48:12
4 Mawu Ofanana  

Ziyoni anamva nakondwera, nasekerera ana aakazi a Yuda; chifukwa cha maweruzo anu, Yehova.