Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 44:8 - Buku Lopatulika

Mwa Mulungu tidzitamanda tsiku lonse, ndipo dzina lanu tidzaliyamika kosatha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mwa Mulungu tidzitamanda tsiku lonse, ndipo dzina lanu tidzaliyamika kosatha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Takhala tikunyadira mphamvu za Mulungu nthaŵi zonse, ndipo tidzakuthokozani mpaka muyaya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Timanyadira mwa Mulungu wathu tsiku lonse, ndipo tidzatamanda dzina lanu kwamuyaya.

Onani mutuwo



Masalimo 44:8
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anawapulumutsa m'dzanja la iye amene anawada, nawaombola kudzanja la mdani.


kuti ulemu wanga uimbire Inu, wosakhala chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzakuyamikani nthawi zonse.


Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.


Mwa Yehova mbeu yonse ya Israele idzalungamitsidwa ndi kudzikuza.


koma wakudzitamandira adzitamandire adzikweze umo, kuti ali wakuzindikira, ndi kundidziwa Ine, kuti ndine Yehova wakuchita zokoma mtima, chiweruziro, ndi chilungamo m'dziko lapansi, pakuti m'menemo ndikondwerera, ati Yehova.


Koma ngati iwe unenedwa Myuda, nukhazikika palamulo, nudzitamandira pa Mulungu,