Masalimo 44:3 - Buku Lopatulika
Pakuti sanalande dziko ndi lupanga lao, ndipo mkono wao sunawapulumutse. Koma dzanja lanu lamanja, ndi mkono wanu, ndi kuunika kwa nkhope yanu. Popeza munakondwera nao,
Onani mutuwo
Pakuti sanalande dziko ndi lupanga lao, ndipo mkono wao sunawapulumutse. Koma dzanja lanu lamanja, ndi mkono wanu, ndi kuunika kwa nkhope yanu. Popeza munakondwera nao,
Onani mutuwo
Iwo sadalande dziko ndi lupanga lao, sadapambane pa nkhondo ndi mphamvu zao. Koma adagonjetsa ndi mphamvu zanu, chifukwa cha kuŵala kwa nkhope yanu, pakuti mudakondwera nawodi.
Onani mutuwo
Sanalande dziko ndi lupanga lawo, si mkono wawo umene unawabweretsera chigonjetso, koma ndi dzanja lanu lamanja, mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu, pakuti munawakonda.
Onani mutuwo