Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 40:13 - Buku Lopatulika

Ndikupemphani, Yehova, ndilanditseni; fulumirani kudzandithandiza, Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndikupemphani, Yehova, ndilanditseni; fulumirani kudzandithandiza, Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Chauta, pulumutseni. Inu Chauta, fulumirani kudzandithandiza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pulumutseni Yehova; Bwerani msanga Yehova kudzandithandiza.

Onani mutuwo



Masalimo 40:13
7 Mawu Ofanana  

Koma Inu, Yehova, musakhale kutali; mphamvu yanga Inu, mufulumire kundithandiza.


Fulumirani kundithandiza, Ambuye, chipulumutso changa.


Mabala anga anunkha, adaola, chifukwa cha kupusa kwanga.


Musandikhalire kutali, Mulungu; fulumirani kundithandiza, Mulungu.