Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 39:4 - Buku Lopatulika

Yehova, mundidziwitse chimaliziro changa, ndi mawerengedwe a masiku anga ndi angati; ndidziwe malekezero anga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova, mundidziwitse chimaliziro changa, ndi mawerengedwe a masiku anga ndi angati; ndidziwe malekezero anga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Inu Chauta, mundidziŵitse mathero a moyo wanga, mundidziŵitse kuchepa kwa masiku anga. Mundilangize kuti moyo wanga sukhalira kutha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Yehova ndionetseni mathero a moyo wanga ndi chiwerengero cha masiku anga; mundidziwitse kuti moyo wanga ndi wosakhalitsa motani.

Onani mutuwo



Masalimo 39:4
4 Mawu Ofanana  

Ha? Mukadandibisa kumanda, mukadandisunga m'tseri, mpaka wapita mkwiyo wanu. Mukadandiikira nthawi, ndi kundikumbukira.


Popeza adziwa mapangidwe athu; akumbukira kuti ife ndife fumbi.


Masiku a mtumiki wanu ndiwo angati? Mudzaweruza liti iwo akundilondola koipa?


Mutidziwitse kuwerenga masiku athu motero, kuti tikhale nao mtima wanzeru.