Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 39:2 - Buku Lopatulika

Ndinatonthola osanena mau, ndinakhala chete osalawa chokoma; ndipo chisoni changa chinabuka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinatonthola osanena mau, ndinakhala chete osalawa chokoma; ndipo chisoni changa chinabuka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero ndidakhala chete osalankhula kanthu, ndidakhala duu, koma popanda phindu, chifukwa mavuto anga ankangokulirakulira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma pamene ndinali chete osanena ngakhale kanthu kalikonse kabwino mavuto anga anachulukirabe.

Onani mutuwo



Masalimo 39:2
10 Mawu Ofanana  

Mundiphunzitse, Yehova, njira ya malemba anu; ndidzaisunga kufikira kutha kwake.


Mundizindikiritse, ndipo ndidzasunga malamulo anu; ndidzawasamalira ndi mtima wanga wonse.


Muike mdindo pakamwa panga, Yehova; sungani pakhomo pa milomo yanga.


Futuka pazoipa, nuchite zabwino, funa mtendere ndi kuulondola.


Iye anatsenderezedwa koma anadzichepetsa yekha osatsegula pakamwa pake; ngati nkhosa yotsogoleredwa kukaphedwa, ndi ngati mwanawankhosa amene ali duu pamaso pa omsenga, motero sanatsegule pakamwa pake.


Musamapatsa chopatulikacho kwa agalu, ndipo musamaponya ngale zanu patsogolo pa nkhumba, kuti zingazipondereze ndi mapazi ao, ndi potembenuka zingang'ambe inu.


pakuti sitingathe ife kuleka kulankhula zimene tinaziona ndi kuzimva.