Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 38:9 - Buku Lopatulika

Ambuye, chikhumbo changa chonse chili pamaso panu; ndipo kubuula kwanga sikubisika kwa Inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ambuye, chikhumbo changa chonse chili pamaso panu; ndipo kubuula kwanga sikubisika kwa Inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ambuye, mumadziŵa zonse zimene ndimakhumba, kusisima kwanga sikuli kosamveka kwa Inu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye, kusisima kwanga sikunabisike kwa Inu.

Onani mutuwo



Masalimo 38:9
8 Mawu Ofanana  

Yehova, mwamva chikhumbo cha ozunzika, mudzakhazikitsa mtima wao, mudzatchereza khutu lanu;


kuti amve kubuula kwa wandende; namasule ana a imfa.


Chifukwa cha liu la kubuula kwanga mnofu wanga umamatika kumafupa anga.


Ndalema nako kuusa moyo kwanga; ndiyandamitsa kama wanga usiku wonse; mphasa yanga ndiolobza ndi misozi yanga.


Natanaele ananena naye, Munandidziwira kuti? Yesu anayankha nati kwa iye, Asanakuitane Filipo, pokhala iwe pansi pa mkuyu paja, ndinakuona iwe.


Pakutinso m'menemo tibuula, ndi kukhumbitsa kuvekedwa ndi chokhalamo chathu chochokera Kumwamba;