Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 38:8 - Buku Lopatulika

Ndafooka ine, ndipo ndachinjizidwa, ndabangula chifukwa cha kumyuka mtima wanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndafooka ine, ndipo ndachinjizidwa, ndabangula chifukwa cha kumyuka mtima wanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndatheratu, ndipo ndatswanyika. Ndikubuula chifukwa cha kuvutika mu mtima.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu; ndikubuwula ndi ululu wa mumtima.

Onani mutuwo



Masalimo 38:8
6 Mawu Ofanana  

Pakuti ndikati ndidye, kumadza kuusa moyo kwanga; ndi kudzuma kwanga kumathiridwa ngati madzi.


M'kati mwanga mupweteka mosapuma, masiku a mazunzo andidzera.


Ndiyenda ndili wothimbirira osati ndi dzuwa ai; ndinyamuka mumsonkhano ndi kufuula.


Pamene ndinakhala chete mafupa anga anakalamba ndi kubuula kwanga tsiku lonse.


Tonse tibangula ngati zilombo, ndi kulira maliro zolimba ngati nkhunda; tiyang'anira chiweruziro koma palibe; tiyang'anira chipulumutso koma chili patali ndi ife.