Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 38:5 - Buku Lopatulika

Mabala anga anunkha, adaola, chifukwa cha kupusa kwanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mabala anga anunkha, adaola, chifukwa cha kupusa kwanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mabala anga aola ndipo akununkha chifukwa cha kupusa kwanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mabala anga akuwola ndipo akununkha chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo.

Onani mutuwo



Masalimo 38:5
8 Mawu Ofanana  

ndipo ndinati, Mulungu wanga, ndigwa nkhope, ndi kuchita manyazi kuweramutsa nkhope yanga kwa inu Mulungu wanga, popeza mphulupulu zathu zachuluka pamutu pathu, ndi kupalamula kwathu kwakula kufikira mu Mwamba.


Pamene ndinakhala chete mafupa anga anakalamba ndi kubuula kwanga tsiku lonse.


Pakuti m'chuuno mwanga mutentha kwambiri; palibe pamoyo m'mnofu mwanga.


Ndikupemphani, Yehova, ndilanditseni; fulumirani kudzandithandiza, Yehova.


Wodala munthuyo mumsankha, ndi kumyandikizitsa, akhale m'mabwalo anu. Tidzakhuta nazo zokoma za m'nyumba yanu, za m'malo oyera a Kachisi wanu.


Mulungu, mudziwa kupusa kwanga; ndipo kutsutsika kwanga sikubisikira Inu.


Kodi mulibe vunguti mu Giliyadi? Kodi mulibe sing'anga m'menemo; analekeranji kuchira mwana wamkazi wa anthu anga?