Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 38:16 - Buku Lopatulika

Pakuti ndinati, Asakondwerere ine; pakuterereka phazi langa, asadzikuze pa ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ndinati, Asakondwerere ine; pakuterereka phazi langa, asadzikuze pa ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Popeza ndimapemphera kuti, “Musalole konse kuti akondwerere pa ine, amene amandinyodola akaona kuti ndikuterereka.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”

Onani mutuwo



Masalimo 38:16
4 Mawu Ofanana  

Pamene ndinati, Literereka phazi langa, chifundo chanu, Yehova, chinandichirikiza.


Kubwezera chilango nkwanga, kubwezera komwe, pa nyengo ya kuterereka phazi lao; pakuti tsiku la tsoka lao layandika, ndi zinthu zowakonzeratu zifulumira kudza.