Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 37:2 - Buku Lopatulika

Pakuti adzawamweta msanga monga udzu, ndipo adzafota monga msipu wauwisi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti adzawamweta msanga monga udzu, ndipo adzafota monga msipu wauwisi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

pakuti mosachedwa amanyala ngati udzu, ndipo amafota ngati masamba aaŵisi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

pakuti monga udzu iwo adzafota msanga, ngati mbewu zobiriwira adzanyala msanga.

Onani mutuwo



Masalimo 37:2
11 Mawu Ofanana  

Atuluka ngati duwa, nafota; athawa ngati mthunzi, osakhalitsa.


chakuti pophuka oipa ngati msipu, ndi popindula ochita zopanda pake; chitero kuti adzaonongeke kosatha.


Koma Inu, Yehova, muli m'mwamba kunthawi yonse.


Pakuti woipayo sadzalandira mphotho; nyali ya amphulupulu idzazima.


Popeza, Anthu onse akunga udzu, ndi ulemerero wao wonse ngati duwa la udzu. Udzuwo ungofota, ndi duwa lake lingogwa;