Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 34:2 - Buku Lopatulika

Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Moyo wanga udzatamanda Yehova; ofatsa adzakumva nadzakondwera.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Moyo wanga umanyadira Chauta. Anthu ozunzika amve ndipo akondwere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Moyo wanga udzanyadira Yehova; anthu osautsidwa amve ndi kukondwera.

Onani mutuwo



Masalimo 34:2
12 Mawu Ofanana  

nati, Ndinatuluka m'mimba ya mai wanga wamaliseche, wamaliseche ndidzamukanso; Yehova anapatsa, Yehova watenga, lidalitsike dzina la Yehova.


Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere.


Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; popeza ndayembekezera mau anu.


Tulutsani moyo wanga m'ndende, kuti ndiyamike dzina lanu; olungama adzandizinga; pakuti mudzandichitira zokoma.


Mwa Mulungu tidzitamanda tsiku lonse, ndipo dzina lanu tidzaliyamika kosatha.


Mwa Yehova mbeu yonse ya Israele idzalungamitsidwa ndi kudzikuza.


koma wakudzitamandira adzitamandire adzikweze umo, kuti ali wakuzindikira, ndi kundidziwa Ine, kuti ndine Yehova wakuchita zokoma mtima, chiweruziro, ndi chilungamo m'dziko lapansi, pakuti m'menemo ndikondwerera, ati Yehova.


kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye.


Koma iye wodzitamandira adzitamandire mwa Ambuye;