Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 33:9 - Buku Lopatulika

Pakuti ananena, ndipo chinachitidwa; analamulira, ndipo chinakhazikika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ananena, ndipo chinachitidwa; analamulira, ndipo chinakhazikika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

pakuti Iye adalankhula, ndipo zidachitikadi, adalamula, ndipo zidaonekadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti Iye anayankhula ndipo zinakhalapo; Iye analamulira ndipo zinakhazikika.

Onani mutuwo



Masalimo 33:9
11 Mawu Ofanana  

Pachiyambi Mulungu adalenga kumwamba ndi dziko lapansi.


Ndipo anati Mulungu, Kuyere; ndipo kunayera.


Zakumwamba zinalengedwa ndi mau a Yehova; ndipo ndi mpweya wa m'kamwa mwake khamu lao lonse.


Mboni zanu zivomerezeka ndithu; chiyero chiyenera nyumba yanu, Yehova, kunthawi za muyaya.


Ndani anganene, chonena chake ndi kuchitikadi, ngati Ambuye salamulira?


ameneyo, pokhala ali chinyezimiro cha ulemerero wake, ndi chizindikiro chenicheni cha chikhalidwe chake, nanyamula zonse ndi mau a mphamvu yake, m'mene adachita chiyeretso cha zoipa, anakhala padzanja lamanja la Ukulu mu Mwamba,


Ndi chikhulupiriro tizindikira kuti maiko ndi a m'mwamba omwe anakonzedwa ndi mau a Mulungu, kotero kuti zinthu zopenyeka sizinapangidwe kuchokera mu zoonekazo.


Muyenera inu, Ambuye wathu, ndi Mulungu wathu, kulandira ulemerero ndi ulemu ndi mphamvu; chifukwa mudalenga zonse, ndipo mwa chifuniro chanu zinakhala, ndipo zinalengedwa.