Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 33:1 - Buku Lopatulika

Fuulani mokondwera mwa Yehova, inu olungama mtima, oongoka mtima ayenera kulemekeza.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Fuulani mokondwera mwa Yehova, inu olungama mtima, oongoka mtima ayenera kulemekeza.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kondwerani mwa Chauta, inu anthu ake. Zoonadi ochita zolungama azitamanda.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imbirani Yehova mokondwera Inu olungama, nʼkoyenera kuti owongoka mtima azitamanda Iyeyo.

Onani mutuwo



Masalimo 33:1
12 Mawu Ofanana  

M'mahema a olungama muli liu lakufuula mokondwera Dzanja lamanja la Yehova ndi la chipulumutso:


Lemekezani Yehova; pakuti Yehova ndiye wabwino; muimbire zolemekeza dzina lake; pakuti nkokondweretsa kutero.


Aleluya; Pakuti kuimbira zomlemekeza Mulungu wathu nkokoma; pakuti chikondweretsa ichi, chilemekezo chiyenera.


Sekerani mwa Yehova, ndimo kondwerani inu olungama mtima; ndipo fuulani mokondwera nonsenu oongoka mtima.


Kondwerani mwa Yehova, olungama inu; ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake.


Nsembe ya oipa inyansa Yehova; koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.


monga kwalembedwa, Palibe mmodzi wolungama, inde palibe mmodzi;


Pakuti monga ndi kusamvera kwa munthu mmodzi ambiri anayesedwa ochimwa, chomwecho ndi kumvera kwa mmodzi ambiri adzayesedwa olungama.


Kondwerani mwa Ambuye nthawi zonse: ndibwerezanso kutero, kondwerani.