Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 30:4 - Buku Lopatulika

Imbirani Yehova, inu okondedwa ake, ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Imbirani Yehova, inu okondedwa ake, ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Imbani nyimbo zotamanda Chauta, inu anthu ake oyera mtima, mumthokoze chifukwa cha dzina lake loyera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika; tamandani dzina lake loyera.

Onani mutuwo



Masalimo 30:4
16 Mawu Ofanana  

Ndipo anaika Alevi ena atumikire ku likasa la Yehova, nalalikire, nayamike, nalemekeze Yehova Mulungu wa Israele.


Atumiza mau ake nawachiritsa, nawapulumutsa ku chionongeko chao.


Ansembe anu avale chilungamo; ndi okondedwa anu afuule mokondwera.


Ndipo anakweza nyanga ya anthu ake, chilemekezo cha okondedwa ake onse; ndiwo ana a Israele, anthu a pafupi pa Iye. Aleluya.


Kwa Inu, Yehova, ndidzafuulira; thanthwe langa, musandikhalire ngati wosamva; pakuti ngati munditontholera ine, ndidzafanana nao iwo akutsikira kumanda.


Sekerani mwa Yehova, ndimo kondwerani inu olungama mtima; ndipo fuulani mokondwera nonsenu oongoka mtima.


Mundisonkhanitsire okondedwa anga, amene anapangana ndi Ine ndi nsembe.


Pakuti chifundo chanu cha pa ine nchachikulu; ndipo munalanditsa moyo wanga kunsi kwa manda.


Kondwerani mwa Yehova, olungama inu; ndipo yamikani pokumbukira chiyero chake.


Afanana ndi Inu ndani mwa milungu, Yehova? Afanana ndi Inu ndani, wolemekezedwa, woyera, woopsa pomyamika, wakuchita zozizwa?


Ndipo wina anafuula kwa mnzake, nati, Woyera, Woyera, Woyera, Yehova wa makamu; dziko lonse lapansi ladzala ulemerero wake.


Ndipo zamoyozo zinai, chonse pa chokha chinali nao mapiko asanu ndi limodzi; ndipo zinadzala ndi maso pozinga ponse ndi m'katimo; ndipo sizipumula usana ndi usiku, ndi kunena, Woyera, woyera, woyera, Ambuye Mulungu Wamphamvuyonse, amene anali, amene ali, ndi amene alinkudza.


Yehova amapha, napatsa moyo; Iye amatsitsa kumanda, naukitsanso.