Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 30:10 - Buku Lopatulika

Mverani, Yehova, ndipo ndichitireni chifundo, Yehova, mundithandize ndi Inu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mverani, Yehova, ndipo ndichitireni chifundo, Yehova, mundithandize ndi Inu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Imvani, Inu Chauta, ndipo mundikomere mtima. Inu Chauta, mukhale mthandizi wanga.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo; Yehova mukhale thandizo langa.”

Onani mutuwo



Masalimo 30:10
7 Mawu Ofanana  

Imvani pemphero langa, Yehova; nditcherere khutu kupemba kwanga; ndiyankheni mwa chikhulupiriko chanu, mwa chilungamo chanu.


Imvani, Yehova, liu langa pofuula ine; mundichitirenso chifundo ndipo mundivomereze.


Yehova ndiye mphamvu yanga, ndi chikopa changa; mtima wanga wakhulupirira Iye, ndipo anandithandiza, chifukwa chake mtima wanga ukondwera kwakukulu; ndipo ndidzamyamika nayo nyimbo yanga.


Taonani, Mulungu ndiye mthandizi wanga, Ambuye ndiye wachirikiza moyo wanga.


Ndalema nako kuusa moyo kwanga; ndiyandamitsa kama wanga usiku wonse; mphasa yanga ndiolobza ndi misozi yanga.