Wodalitsika Yehova, Pakuti adamva mau a kupemba kwanga.
Chauta atamandike, pakuti wamva liwu la kupempha kwanga.
Matamando apite kwa Yehova, popeza Iye wamva kupempha chifundo kwanga.
M'mene ndinasautsika ndinaitanira pa Yehova; anandiyankha nandiika motakasuka Yehova.