Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 27:7 - Buku Lopatulika

Imvani, Yehova, liu langa pofuula ine; mundichitirenso chifundo ndipo mundivomereze.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Imvani, Yehova, liu langa pofuula ine; mundichitirenso chifundo ndipo mundivomereze.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Imvani, Inu Chauta, pamene ndikulira mofuula, mundikomere mtima ndi kundiyankha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova mundichitire chifundo ndipo mundiyankhe.

Onani mutuwo



Masalimo 27:7
8 Mawu Ofanana  

Ndidzati kwa Mulungu, Musanditsutse; mundidziwitse chifukwa cha kutsutsana nane.


Penyani, ndiyankheni, Yehova Mulungu wanga. Penyetsani maso anga, kuti ndingagone tulo ta imfa;


Munasanduliza kulira kwanga kukhale kusekera; munandivula chiguduli changa, ndipo munandiveka chikondwero,


Pakuti moyo wanga watha ndi chisoni, ndi zaka zanga zatha ndi kuusa moyo. Mphamvu yanga yafooka chifukwa cha kusakaza kwanga, ndi mafupa anga apuwala.


Pakufuula ine mundiyankhe, Mulungu wa chilungamo changa; pondichepera mwandikulitsira malo. Ndichitireni chifundo, imvani pemphero langa.


Tamvetsani mau a kufuula kwanga, Mfumu yanga, ndi Mulungu wanga; pakuti kwa Inu ndimapemphera.