Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 27:2 - Buku Lopatulika

Pondifika ine ochita zoipa kudzadya mnofu wanga, inde akundisautsa ndi adani anga, anakhumudwa iwo nagwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pondifika ine ochita zoipa kudzadya mnofu wanga, inde akundisautsa ndi adani anga, anakhumudwa iwo nagwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene adani ndi amaliwongo anga andiputa kuti andiphe, adzaphunthwa ndipo adzagwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane kudzadya mnofu wanga, pamene adani anga ndi achiwembu andithira nkhondo, iwo adzapunthwa ndi kugwa.

Onani mutuwo



Masalimo 27:2
13 Mawu Ofanana  

Mundilondola bwanji ngati Mulungu, losakukwanirani thupi langa?


Ngati amuna a m'hema mwanga sanati, ndani adzapeza munthu wosakhuta nyama yomgawira Yobu?


Adandizinga ngati njuchi; anazima ngati moto waminga; indedi, m'dzina la Yehova ndidzawaduladula.


Kodi onse ochita zopanda pake sadziwa kanthu? Pakudya anthu anga monga akudya mkate, ndipo saitana pa Yehova.


Zingwe za imfa zinandizinga, ndipo mitsinje ya zopanda pake inandiopsa.


Pakuti andizinga agalu, msonkhano wa oipa wanditsekereza; andiboola m'manja anga ndi m'mapazi anga.


Ukani Yehova; ndipulumutseni, Mulungu wanga! Pakuti mwapanda adani anga onse patsaya; mwawathyola mano oipawo.


Kodi ochita zopanda pake sadziwa? Pomadya anthu anga monga akudya mkate; ndipo saitana Mulungu.


Pobwerera m'mbuyo adani anga, akhumudwa naonongeka pankhope panu.


Ndipo ambiri adzaphunthwapo, nagwa, nathyoka, nakodwa, natengedwa.