Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 21:2 - Buku Lopatulika

Mwampatsa iye chikhumbo cha mtima wake, ndipo simunakane pempho la milomo yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mwampatsa iye chikhumbo cha mtima wake, ndipo simunakana pempho la milomo yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwaipatsa zimene mtima wake umakhumba, simudaimane zimene pakamwa pake padapempha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mwayipatsa zokhumba za mtima wake ndipo simunayimane zopempha za pa milomo yake. Sela

Onani mutuwo



Masalimo 21:2
7 Mawu Ofanana  

Udzikondweretsenso mwa Yehova; ndipo Iye adzakupatsa zokhumba mtima wako.


Diso langa lapenya chokhumba ine pa iwo ondilalira, m'makutu mwanga ndamva chokhumba ine pa iwo akuchita zoipa akundiukira.


kuchokera komweko akhoza kupulumutsa konsekonse iwo akuyandikira kwa Mulungu mwa Iye, popeza ali nao moyo wake chikhalire wa kuwapembedzera iwo.


Ndipo Hana anapemphera, nati, Mtima wanga umyuka mokondwera kwa Yehova, nyanga yanga yakwezeka mwa Yehova; pakamwa panga pakula kwa adani anga; popeza ndikondwera m'chipulumutso chanu.