Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 19:6 - Buku Lopatulika

Kutuluka kwake lituluka kolekezera thambo, ndipo kuzungulira kwake lifikira ku malekezero ake; ndipo kulibe kanthu kobisalira kutentha kwake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kutuluka kwake lituluka kolekezera thambo, ndipo kuzungulira kwake lifikira ku malekezero ake; ndipo kulibe kanthu kobisalira kutentha kwake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Limatuluka kuyambira ku mathero ena a thambo, ndi kuzungulira mpaka ku mathero enanso. Palibe chinthu chilichonse chotha kulewa kutentha kwake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo ndi kuzungulira mpaka mbali inanso; palibe chinthu chotha kupewa kutentha kwake.

Onani mutuwo



Masalimo 19:6
7 Mawu Ofanana  

Mitambo ndiyo chomphimba, kuti angaone; ndipo amayenda pa thambo lakumwamba.


Ngati awerengedwa makamu ake? Ndipo ndaniyo, kuunika kwake sikumtulukira?


Chitulukire dzuwa kufikira kulowa kwake lilemekezedwe dzina la Yehova.


Ndikadzitengera mapiko a mbandakucha, ndi kukhala ku malekezero a nyanja;


Inde dzuwa lituluka, nililowa, nilifulumira komwe linatulukako.


ngatitu, mukhalabe m'chikhulupiriro, ochilimika ndi okhazikika ndi osasunthika kulekana nacho chiyembekezo cha Uthenga Wabwino umene mudaumva, wolalikidwa cholengedwa chonse cha pansi pa thambo; umene ine Paulo ndakhala mtumiki wake.


Adani anu onse, Yehova, atayike momwemo. Koma iwo akukonda Inu akhale ngati dzuwa lotuluka mu mphamvu yake. Ndipo dziko linapumula zaka makumi anai.