Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 18:5 - Buku Lopatulika

Zingwe za manda zindizinga, misampha ya imfa inandifikira ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zingwe za manda zindizinga, misampha ya imfa inandifikira ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthambo zakumanda zidandizeŵeza, misampha ya imfa idandikola.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane.

Onani mutuwo



Masalimo 18:5
8 Mawu Ofanana  

Zingwe za imfa zinandizinga, ndi zowawa za manda zinandigwira: ndinapeza nsautso ndi chisoni.


Akadatimiza madziwo, mtsinje ukadapita pa moyo wathu;


Mundiyankhe Yehova; pakuti chifundo chanu nchokoma; munditembenukire monga mwa unyinji wa nsoni zokoma zanu.


Pakuti chifundo chanu cha pa ine nchachikulu; ndipo munalanditsa moyo wanga kunsi kwa manda.


Pakuti munthu sadziwatu mphindi yake; monga nsomba zigwidwa mu ukonde woipa, ndi mbalame zikodwa mumsampha, momwemo ana a anthu amagwidwa ndi nthawi ya tsoka, ngati msampha umene uwagwera modzidzimuka.


yemweyo Mulungu anamuukitsa, atamasula zowawa za imfa, mwakuti sikunali kotheka kuti Iye agwidwe nayo.