Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 18:10 - Buku Lopatulika

Ndipo anaberekeka pa kerubi, nauluka; nauluka msanga pa mapiko a mphepo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anaberekeka pa kerubi, nauluka; nauluka msanga pa mapiko a mphepo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adakwera pa mkerubi nauluka. Adayenda mwaliŵiro ndi mphepo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka; nawuluka ndi mphepo mwaliwiro.

Onani mutuwo



Masalimo 18:10
8 Mawu Ofanana  

Amene alumikiza mitanda ya zipinda zake m'madzi; naika makongwa akhale agaleta ake; nayenda pa mapiko a mphepo.


Weramutsani thambo lanu, Yehova, nimutsike: Khudzani mapiri ndipo adzafuka.


Mbusa wa Israele, tcherani khutu; inu wakutsogolera Yosefe ngati nkhosa; inu wokhala pa akerubi, walitsani.


Yehova ndiye mfumu; mitundu ya anthu injenjemere; Iye akhala pakati pa akerubi; dziko lapansi ligwedezeke.


Ife takhala ngati iwo amene simunawalamulire konse, ngati iwo amene sanatchedwe dzina lanu.