Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 17:11 - Buku Lopatulika

Tsopano anatizinga m'mayendedwe athu, apenyetsetsa m'maso kuti atigwetse pansi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsopano anatizinga m'mayendedwe athu, apenyetsetsa m'maso kuti atigwetse pansi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amangondilondola ndi kundizinga. Amandiyang'ana kuti apeze njira yondigwetsera pansi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Andisaka, tsopano andizungulira ndi maso awo atcheru, kuti andigwetse pansi.

Onani mutuwo



Masalimo 17:11
7 Mawu Ofanana  

Oipa anasolola lupanga, nakoka uta wao; alikhe ozunzika ndi aumphawi, aphe amene ali oongoka m'njira.


Zinandizungulira ngati madzi tsiku lonse; zinandizinga pamodzi.


Ndipo Saulo anamuka mbali ina ya phiri, Davide ndi anthu ake kuseri kwake; ndipo Davide anafulumira kuthawa, chifukwa cha kuopa Saulo; popeza Saulo ndi anthu ake anazinga Davide ndi anthu ake kwete kuti awagwire.