Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 149:8 - Buku Lopatulika

kumanga mafumu ao ndi maunyolo, ndi omveka ao ndi majerejede achitsulo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kumanga mafumu ao ndi maunyolo, ndi omveka ao ndi majerejede achitsulo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amange mafumu ao ndi maunyolo, amange atsogoleri ao ndi zitsulo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kumanga mafumu awo ndi zingwe, anthu awo otchuka ndi unyolo wachitsulo,

Onani mutuwo



Masalimo 149:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo akamangidwa m'nsinga, nakakodwa ndi zingwe za mazunzo,


Ndipo awa ndi mafumu a dzikolo amene Yoswa ndi ana a Israele anawakantha tsidya lija la Yordani kumadzulo, kuyambira Baala-Gadi m'chigwa cha Lebanoni mpaka phiri la Halaki lokwera kunka ku Seiri; ndipo Yoswa analipereka kwa mafuko a Israele, likhale laolao, monga mwa magawo ao;