Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 149:7 - Buku Lopatulika

kubwezera chilango akunja, ndi kulanga mitundu ya anthu;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kubwezera chilango akunja, ndi kulanga mitundu ya anthu;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kuti alipsire mafuko achikunja, kuti alange mitundu ina ya anthu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kubwezera chilango anthu a mitundu ina, ndi kulanga anthu a mitundu yonse,

Onani mutuwo



Masalimo 149:7
12 Mawu Ofanana  

Nasonkhana pamodzi Ayuda ena okhala m'maiko a mfumu, nalimbikira moyo wao, napumula pa adani ao, nawapha a iwo odana nao zikwi makumi asanu ndi awiri mphambu zisanu; koma sanalande zofunkha.


ndiwo masiku amene Ayuda anapumula pa adani ao; ndi mwezi wachisoni unawasandulikira wakukondwera, ndi wamaliro ukhale tsiku lokoma, awayese masiku amadyerero ndi akukondwera, akutumizirana magawo, ndi akupatsa zaufulu kwa osauka.


Ndipo ndidzazula zifanizo zako m'kati mwako, ndi kutha mizinda yako.


Ndipo atatero, Yoswa anawakantha nawapha, nawapachika pa mitengo isanu; nalikupachikidwa pa mitengo mpaka madzulo.


Mutemberere Merozi, ati mthenga wa Yehova, mutemberere chitemberere nzika zake; pakuti sanadzathandize Yehova, kumthandiza Yehova pa achamuna.